Proverbs 21:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuli bwino kukhala potero pa denga kupambana kukhala m'nyumba pamodzi ndi mkazi wolongolola.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kukhala pangodya ya tsindwi kufunika kuposa kukhala m'nyumba ndi mkazi wolongolola.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼkwabwino kukhala wekha pa ngodya ya denga la nyumba, kuposa kukhala mʼnyumba pamodzi ndi mkazi wolongolola.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kukhala pa ngondya ya tsindwi kufunika Kuposa kukhala m'nyumba ndi mkazi wolongolola.