Proverbs 22:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kupusa kumakhala mumtima mwa mwana, koma ndodo yomlangira mwanayo idzachotsa kupusako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Utsiru umangidwa mumtima mwa mwana; koma nthyole yomlangira idzauingitsira kutali.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Uchitsiru umakhala mu mtima mwa mwana, koma ndodo yomulangira mwanayo idzachotsa uchitsiruwo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Utsiru umangidwa mumtima mwa mwana; Koma ntyole yomlangira idzauingitsira kutari.