Proverbs 22:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana muzimuphunzitsa njira yoti aziyendamo, ndipo atakalamba sadzachokamo m'njira imeneyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Phunzitsa mwana poyamba njira yake; ndipo angakhale atakalamba sadzachokamo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana muzimuphunzitsa njira yake, ndipo akadzakalamba sadzachokamo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Phunzitsa mwana poyamba njira yace; Ndipo angakhale atakalamba sadzacokamo.