Proverbs 22:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene ali ndi diso lachifundo adzadalitsidwa, poti amagaŵana chakudya chake ndi anthu osauka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwini diso lamataya adzadala; pakuti apatsa osauka zakudya zake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amene ali ndi diso lachifundo adzadalitsika, pakuti iye amagawana chakudya chake ndi anthu osauka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwini diso lamataya adzadala; Pakuti apatsa osauka zakudya zace.