Proverbs 23:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usakhale pakati pa anthu amene amaledzera, kapena pakati pa anthu odya nyama mwadyera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usakhale mwa akumwaimwa vinyo, ndi ankhuli osusuka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usakhale pakati pa anthu amene amaledzera kapena pakati pa anthu amene amadya nyama mwadyera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usakhale mwa akumwaimwa vinyo, Ndi ankhuli osusuka.