Proverbs 23:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usatengeke mtima ndi kufiira kwa vinyo, pamene akututuma m'chikho namakoma poloŵa ku m'mero.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usayang'ane pavinyo alikufiira, alikung'azimira m'chikho, namweka mosalala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usatengeke mtima ndi kufiira kwa vinyo, pamene akuwira mʼchikho pamene akumweka bwino!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usayang'ane pavinyo alikufiira. Alikung'azimira m'cikho. Namweka mosalala.