Proverbs 23:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usadzitopetse nkufuna chuma, udziŵe kuchita zinthu mwanzeru ndi kudziletsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usadzitopetse kuti ulemere; leka nzeru yakoyako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usadzitopetse wekha ndi kufuna chuma, ukhale ndi nzeru ya kudziretsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usadzitopetse kuti ulemere; Leka nzeru yako yako.