Proverbs 24:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ukataya mtima pamene upeza zovuta, ndiye kuti mphamvu zako ndi zochepa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ukalefuka tsiku la tsoka mphamvu yako ichepa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati utaya mtima nthawi ya mavuto ndiye kuti mphamvu yako ndi yochepadi!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ukalefuka tsiku la tsoka Mphamvu yako icepa.