Proverbs 24:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma aweruzi amene amalanga anthu oipa adzapeza bwino, ndipo adzakhala ndi madalitso ambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Omwe amdzudzula adzasekera, nadzadalitsika ndithu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma olanga anthu oyipa zinthu zidzawayendera bwino ndipo madalitso ochuluka adzakhala pa iwo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Omwe amdzudzula adzasekera, Nadzadalitsika ndithu.