Proverbs 24:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nyumba imamangidwa ndi anthu anzeru, ndipo imakhazikika ndi anthu a mtima wodziŵa zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nzeru imangitsa nyumba; luntha liikhazikitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nyumba imamangidwa ndi anthu anzeru, ndipo imakhazikika ndi anthu odziwa zinthu;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nzeru imangitsa nyumba; Luntha liikhazikitsa.