Proverbs 24:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono nditaona, ndidayamba kuganizirapo pa zimenezo, nditayang'ana, ndidatolapo phunziro ili:
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo ndinayang'ana ndi kuganizira, ndinaona ndi kulandira mwambo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono nditaona ndinayamba kuganizira mu mtima mwanga ndipo ndinatolapo phunziro ili:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo ndinayang'ana ndi kuganizira, Ndinaona ndi kulandira mwambo.