Proverbs 25:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
kuwopa kuti wina akamva mau ako, angakuchititse manyazi, ndipo mbiri yako yoipa sidzatha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti wakumva angakutonze, mbiri yako yoipa ndi kusachoka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuopa kuti wina akamva mawu ako adzakuchititsa manyazi ndipo mbiri yako yoyipa sidzatha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kuti wakumva angakutonze, Mbiri yako yoipa ndi kusacoka.