Proverbs 25:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kwa anthu amene amtuma, wamthenga wokhulupirika ali ngati madzi ozizira pa nthaŵi yotentha, amaziziritsa mtima wa mbuyake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga chisanu cha chipale chofewa pa nthawi ya masika, momwemo mthenga wokhulupirika kwa amene anamtuma; atsitsimutsa moyo wa ambuyake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wamthenga wodalirika ali ngati madzi ozizira pa nthawi yokolola kwa anthu amene amutuma; iye amaziziritsa mtima bwana wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga cisanu ca cipale cofewa pa nthawi ya masika, Momwemo mthenga wokhulupirika kwa amene anamtuma; Atsitsimutsa moyo wa ambuyace.