Proverbs 25:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wonyadira mphatso imene saipereka, ali ngati mitambo ndi mphepo zopanda mvula.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga mitambo ndi mphepo popanda mvula, momwemo ndiye wodzikweza ndi zipatso zake monyenga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wonyadira mphatso imene sayipereka ali ngati mitambo ndi mphepo yopanda mvula.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga mitambo ndi mphepo popanda mvula, Momwemo ndiye wodzikweza ndi zipatso zace monyenga.