Proverbs 25:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ukapeza uchi, ingodya wokukwanira, kuwopa kuti ungakoledwe nawo nkuyamba kusanza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wapeza uchi kodi? Idyapo wokwanira, kuti ungakukole, nusanze.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati upeza uchi, ingodya okukwanira, kuopa ungakoledwe nawo ndi kuyamba kusanza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wapeza uci kodi? Idyapo wokwanira, Kuti ungakukole, nusanze.