Proverbs 25:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kunyumba kwa mnzako uzipitako kamodzikamodzi, kuwopa kuti angatope nawe, nkuyamba kudana nawe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Phazi lako lilowe m'nyumba ya mnzako kamodzikamodzi; kuti angatope nawe ndi kukuda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Uzipita kamodzikamodzi ku nyumba ya mnzako ukawirikiza kupita, udzadana naye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Phazi lako lilowe m'nyumba ya mnzako kamodzi kamodzi; Kuti angatope nawe ndi kukuda.