Proverbs 25:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wochitira mnzake umboni wonama, amapweteka mnzakeyo ngati chibonga kapena lupanga kapena muvi wakuthwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wochitira mnzake umboni wonama ndiye chibonga, ndi lupanga, ndi muvi wakuthwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wochitira mnzake umboni wonama, ali ngati chibonga kapena lupanga kapena muvi wakuthwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wocitira mnzace umboni wonama Ndiye cibonga, ndi lupanga, ndi mubvi wakuthwa.