Proverbs 25:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mdani wako akakhala ndi njala, umpatse chakudya, akamva ludzu, umpatse madzi akumwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mdani wako akamva njala umdyetse, akamva ludzu ummwetse madzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya kuti adye; ngati ali ndi ludzu mupatse madzi kuti amwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mdani wako akamva njala umdyetse, Akamva ludzu ummwetse madzi,