Proverbs 25:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wabwino amene amagonjera munthu woipa amafanafana ndi kasupe wodzaza ndi matope kapena chitsime cha madzi oipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga kasupe wopondedwa, ndi chitsime choonongeka, momwemo wolungama ngati agonjera woipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wolungama amene amagonjera munthu woyipa ali ngati kasupe wodzaza ndi matope kapena chitsime cha madzi oyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga kasupe wopondedwa, ndi citsime cobvonongeka, Momwemo wolungama ngati akonjera woipa.