Proverbs 25:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Si kwabwino kudya uchi wambiri, tsono muchenjere nawo mau oyamikira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kudya uchi wambiri sikuli kwabwino; chomwecho kufunafuna ulemu wakowako sikuli ulemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sibwino kudya uchi wambiri, sibwinonso kudzifunira wekha ulemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kudya uci wambiri sikuli kwabwino; Comweco kufunafuna ulemu wako wako sikuli ulemu.