Proverbs 25:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wosadzimanga mtima ali ngati mzinda umene adani authyola nkuusiya wopanda malinga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wosalamulira mtima wake akunga mudzi wopasuka wopanda linga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amene samatha kudziretsa ali ngati mzinda umene adani awuthyola ndi kuwusiya wopanda malinga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wosalamulira mtima wace Akunga mudzi wopasuka wopanda linga,