Proverbs 25:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga momwe uliri mlengalenga kutalika, ndi momwe liliri dziko lapansi kuzama, ndi m'mene aliri maganizo a mfumu kusadziŵika kwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamlengalenga patalika, ndi padziko pakuya, koma mitima ya mafumu singasanthulike.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga momwe kwatalikira kumwamba ndi momwe kulili kuzama kwa dziko lapansi, ndi momwemonso alili maganizo a mfumu kusadziwika kwake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamlengalenga patarika, ndi padziko pakuya, Koma mitima ya mafumu singasanthulike.