Proverbs 25:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pajatu kuli bwino kuchita kukuuza kuti, “Dzakhale pokwera pano”, koposa kuchita kukutsitsa chifukwa cha wina wokupambana. Zimene maso ako azipenya,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti kunena kwa iwe, Takwera kuno, kupambana ndi kuti utsitsidwe pamaso pa kalonga, amene maso ako anamuona.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
paja ndi bwino kuti mfumu ichite kukuwuza kuti, “Bwera pamwamba pano,” kulekana ndi kuti ikuchititse manyazi chifukwa cha wina wokuposa. Chimene wachiona ndi maso ako,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti kunena kwa iwe, Takwera kuno, Kupambana ndi kuti utsitsidwe pamaso pa kalonga, Amene maso ako anamuona.