Proverbs 25:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
usafulumire kupita nazo ku bwalo lamilandu, chifukwa udzatani nanga pambuyo pake, ngati mnzako akuchititsa manyazi pokutsutsa?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usatuluke mwansontho kukalimbana, ungalephere pa kutha kwake, atakuchititsa mnzako manyazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
usafulumire kupita nacho ku bwalo la milandu nanga udzachita chiyani pa mapeto pake ngati mnansi wako adzakuchititsa manyazi?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usaturuke mwansontho kukalimbana, Ungalephere pa kutha kwace, Atakucititsa mnzako manyazi.