Proverbs 25:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mnzako uzichita kukamba naye zinthu, ndipo usaulule chinsinsi cha wina,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nena mlandu wako ndi mnzako, osawulula zinsinsi za mwini;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kamba mlandu ndi mnansi wako, koma osawulula chinsinsi cha munthu wina
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nena mlandu wako ndi mnzako, Osaulula zinsinsi za mwini;