Proverbs 26:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ulemu woulandira chitsiru uli ngati chisanu chambee chomagwa nthaŵi yachilimwe, kapena mvula yomagwa nthaŵi yokolola.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga chipale chofewa m'malimwe, ndi mvula m'masika, momwemo ulemu suyenera chitsiru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati chisanu choti mbee nthawi yachilimwe kapena mvula nthawi yokolola, ndi momwe zilili ndi ulemu wowulandira chitsiru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga cipale cofewa m'malimwe, ndi mvula m'masika, Momwemo ulemu suyenera citsiru.