Proverbs 26:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene amalemba ntchito chitsiru chongodziyendera kapena chidakwa, ali ngati munthu woponya mivi amene amangolasa anthu chilaselase.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga woponya mivi ndi kulasa onse, momwemo wolembera chitsiru, ndi wolembera omwe alikupita panjira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amene amalemba ntchito chitsiru chongoyendayenda, ali ngati woponya mivi amene angolasa anthu chilaselase.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga woponya mibvi ndi kulasa onse, Momwemo wolembera citsiru, ndi wolembera omwe alikupita panjira.