Proverbs 26:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale chitsiru chomwe nkuti ndiponi, pali chikhulupiriro, koma osati munthu wodziyesa wanzeru pamene ali wopusa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi uona munthu wodziyesa wanzeru? Ngakhale chitsiru chidzachenjera koma ameneyo ai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wa uchitsiru aliko bwino popeza pali chiyembekezo kuposana ndi munthu amene amadziyesa yekha kuti ndi wanzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi uona munthu wodziyesa wanzeru? Ngakhale citsiru cidzacenjera koma ameneyo ai.