Proverbs 26:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Waulesi amati, “Pali mkango pa njira! Mumseumo muli mkango!”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Waulesi ati, Mkango uli panjira, wobangulawo uli m'makwalala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu waulesi amati, “Mu msewu muli mkango, mkango woopsa ukuyendayenda mʼmisewu!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wolesi ati, Mkango uli panjira, Wobangulawo uli m'makwalala.