Proverbs 26:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Waulesi amati akapisa dzanja lake m'mbale, kumamtopetsa kuti alifikitse kukamwa kwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Waulesi alonga dzanja lake m'mbale; kumtopetsa kulibweza kukamwa kwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu waulesi akapisa dzanja lake mu mʼbale; zimamutopetsa kuti alifikitse pakamwa pake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wolesi alonga dzanja lace m'mbale; Kumtopetsa kulibweza kukamwa kwace.