Proverbs 26:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene angoloŵerera ndeu ya eniake, ali ngati munthu wombwandira galu wongodziyendera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wakungopita ndi kuvutika ndi ndeu yosakhala yake akunga wogwira makutu a galu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wongolowera mikangano imene si yake ali ngati munthu wogwira makutu a galu wongodziyendera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wakungopita ndi kubvutika ndi ndeu yosakhala yace Akunga wogwira makutu a garu.