Proverbs 26:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga munthu wopenga amene amangoponya nsakali zamoto, kapena mivi yoopsa,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga woyaluka woponya nsakali, mivi, ndi imfa,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga munthu wamisala amene akuponya sakali zamoto kapena mivi yoopsa,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga woyaruka woponya nsakali, Mibvi, ndi imfa,