Proverbs 26:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
ndimonso amakhalira munthu wonyenga mnzake, amene amati, “Ai, ndi zoseka chabe!”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
momwemo wonyenga mnzake ndi kuti, ndi kusewera kumeneku.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndi momwe alili munthu wonamiza mnzake, amene amati, “Ndimangoseka chabe!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Momwemo wonyenga mnzace ndi kuti, Ndi kusewera kumeneku.