Proverbs 26:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga imachitira mpheta yokhalira kuuluka, monga amachitira namzeze kumangoti zwezwezwe, ndimonso limachitira temberero lopanda chifukwa, silitha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga mpheta ilikuzungulira, ndi namzeze alikuuluka, momwemo temberero la pachabe silifikira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati timba wokhalira kuwuluka kapena namzeze wokhalira kuzungulirazungulira, ndi mmenenso limachitira temberero lopanda chifukwa, silichitika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga mpheta irikuzungulira, ndi namzeze alikuuluka, Momwemo temberero la pacabe silifikira.