Proverbs 26:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga momwe aliri makala pa moto wonyeka ndiponso nkhuni pa moto woyaka, ndimonso amakhalira munthu wandeu poutsa mikangano.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga makala ozizira pa makala akunyeka, ndi nkhuni pamoto; momwemo munthu wamakangano autsa ndeu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga alili makala pa moto wonyeka kapena mmene zimachitira nkhuni pa moto, ndi mmene alili munthu wolongolola poyambitsa mikangano.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga makala ozizira pa makala akunyeka, ndi nkhuni pamoto; Momwemo munthu wamakangano autsa ndeu.