Proverbs 26:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wachidani pakamwa pake pamalankhula zabwino, pamene mumtima mwake muli zonyenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wakuda mnzake amanyenga ndi milomo yake; koma akundika chinyengo m'kati mwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wachidani amayankhula zabwino pamene mu mtima mwake muli chinyengo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wakuda mnzace amanyenga ndi milomo yace; Koma akundika cinyengo m'kati mwace;