Proverbs 26:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Woteroyo akamalankhula mokometsa mau, usamkhulupirire, pakuti mumtima mwake mwadzaza zoipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene akometsa mau ake usamkhulupirire; pakuti m'mtima mwake muli zonyansa zisanu ndi ziwiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale wotereyu mawu ake ali okoma, koma usamukhulupirire, pakuti mu mtima mwake mwadzaza zonyansa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene akometsa mau ace usamkhulupirire; Pakuti m'mtima mwace muli zonyansa zisanu ndi ziwiri.