Proverbs 26:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chitsiru usamachiyankha potsata uchitsiru wake, kuwopa kuti ungafanefane nacho.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usayankhe chitsiru monga mwa utsiru wake, kuti ungafanane nacho iwe wekha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usayankhe chitsiru monga mwa uchitsiru wake, kuopa kuti ungadzakhale ngati chitsirucho.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usayankhe citsiru monga mwa utsiru wace, Kuti ungafanane naco iwe wekha.