Proverbs 26:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma mwina uzichiyankha chitsiru potsata uchitsiru wake, kuwopa kuti chingamadziyese chanzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yankha chitsiru monga mwa utsiru wake, kuti asadziyese wanzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma nthawi zina umuyankhe monga mwa uchitsiru wake, kuopa kuti angamadziyese yekha wanzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yankha citsiru monga mwa utsiru wace, Kuti asadziyese wanzeru.