Proverbs 26:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene amatuma chitsiru kukanena uthenga, amachita ngati kudzidula mapazi ndipo amadziitanira mavuto.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wotumiza mau ndi dzanja la chitsiru adula mapazi ake, namwa zompweteka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kutuma chitsiru kuti akapereke uthenga kuli ngati kudzidula mapazi ndipo kumakuyitanira mavuto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wotumiza mau ndi dzanja la citsiru Adula mapazi ace, namwa zompweteka.