Proverbs 26:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga imachitira minga yobaya dzanja la chidakwa ndimonso umakhalira mwambi m'kamwa mwa zitsiru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga munga wolasa dzanja la woledzera, momwemo mwambi m'kamwa mwa zitsiru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga umachitira mtengo waminga wobaya mʼdzanja la chidakwa ndi mmene ulili mwambi mʼkamwa mwa chitsiru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga munga wolasa dzanja la woledzera, Momwemo mwambi m'kamwa mwa zitsiru.