Proverbs 27:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usamanyadira zamaŵa, pakuti sudziŵa zimene zidzachitika pa tsikulo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usanyadire zamawa, popeza sudziwa tsiku lina lidzabala chiyani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usamanyadire za mawa, pakuti sudziwa zimene zidzachitike pa tsikulo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usanyadire zamawa, Popeza sudziwa tsiku lina lidzabala ciani?