Proverbs 27:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga momwe nkhope imaonekera m'madzi, momwemonso mtima wa munthu umadziŵika ndi zochita zake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga m'madzi nkhope zionana, momwemo mitima ya anthu idziwana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga momwe nkhope imaonekera mʼmadzi, chomwechonso mtima wa munthu umadziwika ndi ntchito zake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga m'madzi nkhope zionana, Momwemo mitima ya anthu idziwana.