Proverbs 27:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu amene wasokera kutali ndi kwao, ali ngati mbalame yosokera kutali ndi chisa chake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga mbalame yosochera kuchisa chake, momwemo munthu wosochera kumalo ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amene wasochera ku nyumba kwake, ali monga mbalame imene yasochera pa chisa chake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga mbalame yosocera ku cisa cace, Momwemo munthu wosocera ku malo ace.