Proverbs 28:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Woipa mtima amangodzithaŵira popanda wina wompirikitsa, koma wochita zabwino amalimba mtima ngati mkango.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Woipa athawa palibe momthamangitsa; koma olungama alimba mtima ngati mkango.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu woyipa amathawa ngakhale palibe wina womuthamangitsa, koma wolungama ndi wolimba mtima ngati mkango.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Woipaathawapalibewomthamangitsa; Koma olungama alimba mtima ngati mkango.