Proverbs 28:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene amapatsa osauka sadzasoŵa kanthu koma amene amatsinzina dala kuti asaŵapenye, adzatembereredwa kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wogawira aumphawi sadzasowa; koma wophimba maso ake adzatembereredwa kwambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amene amapereka kwa osauka sadzasowa kanthu, koma amene amatsinzina maso ake adzatembereredwa kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wogawira aumphawi sadzasowa; Koma wophimba maso ace adzatembereredwa kwambiri.