Proverbs 29:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kunyada kwa munthu kudzamtsitsa, koma amene ali wodzichepetsa adzalandira ulemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kudzikuza kwa munthu kudzamchepetsa; koma wokhala ndi mtima wodzichepetsa adzalemekezedwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kunyada kwa munthu kudzamutsitsa, koma munthu wodzichepetsa amalandira ulemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kudzikuza kwa munthu kudzamcepetsa; Koma wokhala ndi mtima wodzicepetsa adzalemekezedwa.