Proverbs 29:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Woyenda ndi mbala ndi wodana ndi moyo wake, amamva kutemberera, koma osaulula kanthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Woyenda ndi mbala ada moyo wakewake; amva kulumbira, koma osawulula kanthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Woyenda ndi munthu wakuba ndi mdani wa moyo wake womwe; amalumbira koma osawulula kanthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Woyenda ndi mbala ada moyo wace wace; Amva kulumbira, koma osaulula kanthu.