Proverbs 3:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wanga, usaiŵale malangizo angaŵa, koma mtima wako usunge malamulo anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwananga, usaiwale malamulo anga, mtima wako usunge malangizo anga;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wanga, usayiwale malangizo anga, mtima wako usunge malamulo anga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwananga, usaiwale malamulo anga, Mtima wako usunge malangizo anga;