Proverbs 3:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ukatero, nkhokwe zako zidzadzaza ndi dzinthu dzambiri, mbiya zako zidzachita kusefukira ndi vinyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
motero nkhokwe zako zidzangoti thee, mbiya zako zidzasefuka vinyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ukatero nkhokwe zako zidzadzaza ndi zinthu zambiri, ndiponso mitsuko yako idzadzaza ndi vinyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Motero nkhokwe zako zidzangoti the, Mbiya zako zidzasefuka vinyo.